1 Taonani, mkono wa Yehova si waufupi kuti sungathe kupulumutsa,
2 Koma zoyipa zanu zakulekanitsani
3 Pakuti manja anu ali psuu ndi magazi.
4 Palibe amene akuyimba mnzake mlandu molungama,
5 Iwo amayikira mazira a mamba
6 Ukonde wawo wa kangawude sangawuvale ngati chovala;
7 Amathamangira kukachita zoyipa;
8 Iwo sadziwa kuchita za mtendere;
9 Anthu akuti, “Chifukwa cha zimenezi chilungamo chatitalikira;
10 Timapapasapapasa khoma ngati munthu wosaona,
11 Tonse timabangula ngati zimbalangondo:
12 Pakuti zolakwa zathu nʼzochuluka pamaso panu,
13 Tawukira ndi kumukana Yehova.
14 Motero kuweruza kolungama kwalekeka
15 Choonadi sichikupezeka kumeneko,
16 Yehova anaona kuti panalibe ndi mmodzi yemwe,
17 Iye anavala chilungamo ngati chovala chachitsulo chapachifuwa,
18 Iye adzawabwezera chilango adani a anthu ake
19 Choncho akadzabwera ngati madzi
20 “Mpulumutsi adzabwera ku Ziyoni
21 Yehova akuti, “Kunena za pangano lake ndi iwo, Mzimu wanga umene uli pa inu, ndiponso mawu anga amene ndayika mʼkamwa mwanu sadzachoka mʼkamwa mwanu, kapena kuchoka mʼkamwa mwa ana anu, kapena mʼkamwa mwa zidzukulu zawo kuyambira tsopano mpaka kalekale,”