Isaías 57

NYA

1 Anthu olungama amafa,

2 Iwo amene amakhala moyo wolungama

3 “Bwerani kuno, anthu ochita zoyipa,

4 Kodi inu mukuseka yani?

5 Inu mumapembedza mafano pamene mumalobodoka ndi zilakolako zanu pakati pa mitengo ya thundu,

6 Mafano a pakati pa miyala yosalala ya mu zigwa ndiye chuma chanu. Inde, ndiye gawo lanu.

7 Inu munayiwala bedi lanu pa phiri lalitali ndi looneka kutali.

8 Mʼnyumba mwanu mwayika

9 Mumapita kukapembedza fano la Moleki mutatenga mafuta

10 Inu mumatopa ndi maulendo anu,

11 “Kodi ndani amene mwachita naye mantha ndi kumuopa,

12 Koma ndaonetsa poyera ntchito zanu zomwe mumati nʼzolungama,

13 Pamene mufuwula kupempha thandizo,

14 Ndipo panamveka mawu akuti,

15 Pakuti Iye amene ali Wamkulu ndi Wopambanazonse,

16 Sindidzawatsutsa anthu mpaka muyaya

17 Ine ndinakwiya kwambiri chifukwa cha tchimo lawo ladyera;

18 Ndaona zochita zawo, komabe ndidzawachiritsa;

19 anthu olira a mu Israeli adzanditamanda ndi milomo yawo.

20 Koma anthu oyipa ali ngati nyanja yowinduka,

21 “Palibe mtendere kwa oyipa,” akutero Mulungu wanga.

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado