Isaías 56

NYA

1 Yehova akuti,

2 Ndi wodala munthu amene amachita zimenezi,

3 Mlendo amene waphatikana ndi Yehova asanene kuti,

4 Popeza Yehova akuti,

5 ndidzawapatsa dzina ndi mbiri yabwino

6 Yehova akuti, “Alendo amene amadziphatika kwa Yehova,

7 amenewa Ine ndidzawafikitsa ku phiri langa lopatulika,

8 Ambuye Yehova, amene amasonkhanitsa

9 Bwerani, inu zirombo zonse zakuthengo,

10 Atsogoleri onse a Israeli ndi akhungu,

11 Ali ngati agalu amene ali ndi njala yayikulu;

12 Aliyense amafuwulira mnzake kuti, “Bwera, tiye timwe vinyo!

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado