1 Mverani Ine, inu anthu a pa zilumba
2 Iye anasandutsa pakamwa panga kukhala ngati lupanga lakuthwa,
3 Iye anati kwa ine, “Ndiwe mtumiki wanga, Israeli.
4 Koma Ine ndinati, “Ine ndinkaganiza kuti ndinagwira ntchito
5 Yehova anandiwumba ine
6 Yehovayo tsono akuti,
7 Yehova Mpulumutsi ndi Woyerayo wa Israeli akuyankhula,
8 Yehova akuti,
9 Ndidzawuza a mʼndende kuti atuluke
10 Iwo sadzamva njala kapena ludzu,
11 Mapiri anga onse ndidzawasandutsa njira yoyendamo,
12 Taonani, anthu anga adzachokera kutali,
13 Imbani mwachimwemwe, inu zolengedwa zamlengalenga;
14 Koma Ziyoni anati, “Yehova wandisiya,
15 “Kodi amayi angathe kuyiwala mwana wawo wakubere
16 Taona, ndakulemba iwe mʼzikhantho zanga;
17 Amisiri odzakumanganso akubwerera mofulumira,
18 Kweza maso ako ndipo uyangʼaneyangʼane
19 “Ngakhale unasanduka bwinja ndi kuwonongedwa
20 Ana obadwa nthawi yako yachisoni
21 Tsono iwe udzadzifunsa kuti,
22 Zimene Ambuye Yehova akunena ndi izi,
23 Mafumu adzakhala abambo wongokulera
24 Kodi mungathe kulanda anthu ankhondo zofunkha zawo,
25 Koma zimene Yehova akunena ndi izi,
26 Anthu amene anakuponderezani adzadya mnofu wawo omwe;