1 “Mverani izi, inu nyumba ya Yakobo,
2 Komabe inu mumadzitcha nzika za mzinda wopatulika
3 Zimene zinachitika poyamba ndinalosera kalekale,
4 Pakuti Ine ndinadziwa kuti iwe ndiwe nkhutukumve
5 Ine ndinakuwuziratu zinthu izi kalekale lomwe;
6 Inu munamva zinthu zimenezi.
7 Zinthu zimenezi zikulengedwa tsopano lino, osati kalekale;
8 Inu simunazimvepo kapena kuzidziwa;
9 Ine ndikuchedwetsa mkwiyo wanga chifukwa cha dzina langa.
10 Taonani, ndinakuyeretsani ngati siliva;
11 Chifukwa cha ulemu wanga, chifukwa cha ulemu wanga Ine ndikuchita zimenezi.
12 “Tamvera Ine, iwe Yakobo,
13 Inde dzanja langa linamanga maziko a dziko lapansi,
14 “Sonkhanani pamodzi inu nonse ndipo mvetserani:
15 Ine, Inetu, ndayankhula;
16 “Bwerani pafupi ndipo mvetserani izi:
17 Yehova, Mpulumutsi wanu,
18 Ngati iwe ukanangosamalira zolamulira zanga,
19 Zidzukulu zako zikanachuluka ngati mchenga,
20 Tulukani mʼdziko la Babuloni!
21 Iwo sanamve ludzu pamene Yehova ankawatsogolera mʼchipululu;
22 “Palibe mtendere kwa anthu ochimwa,” akutero Yehova.