Isaías 48

NYA

1 “Mverani izi, inu nyumba ya Yakobo,

2 Komabe inu mumadzitcha nzika za mzinda wopatulika

3 Zimene zinachitika poyamba ndinalosera kalekale,

4 Pakuti Ine ndinadziwa kuti iwe ndiwe nkhutukumve

5 Ine ndinakuwuziratu zinthu izi kalekale lomwe;

6 Inu munamva zinthu zimenezi.

7 Zinthu zimenezi zikulengedwa tsopano lino, osati kalekale;

8 Inu simunazimvepo kapena kuzidziwa;

9 Ine ndikuchedwetsa mkwiyo wanga chifukwa cha dzina langa.

10 Taonani, ndinakuyeretsani ngati siliva;

11 Chifukwa cha ulemu wanga, chifukwa cha ulemu wanga Ine ndikuchita zimenezi.

12 “Tamvera Ine, iwe Yakobo,

13 Inde dzanja langa linamanga maziko a dziko lapansi,

14 “Sonkhanani pamodzi inu nonse ndipo mvetserani:

15 Ine, Inetu, ndayankhula;

16 “Bwerani pafupi ndipo mvetserani izi:

17 Yehova, Mpulumutsi wanu,

18 Ngati iwe ukanangosamalira zolamulira zanga,

19 Zidzukulu zako zikanachuluka ngati mchenga,

20 Tulukani mʼdziko la Babuloni!

21 Iwo sanamve ludzu pamene Yehova ankawatsogolera mʼchipululu;

22 “Palibe mtendere kwa anthu ochimwa,” akutero Yehova.

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado