1 “Tsika, ndi kukhala pa fumbi,
2 Tenga mphero ndipo upere ufa;
3 Maliseche ako adzakhala poyera
4 Woyerayo wa Israeli ndiye Mpulumutsi wathu,
5 “Khala chete, ndipo lowa mu mdima,
6 Ndinawakwiyira anthu anga,
7 Iwe unati, ‘Ine ndidzakhalapo nthawi zonse
8 “Ndipo tsopano, tamvera, iwe wongokonda zokondweretsawe,
9 Koma mʼkamphindi, ndiponso tsiku limodzi,
10 Iwe unkadalira kuyipa kwako
11 Ngozi yayikulu idzakugwera
12 “Pitiriza tsono kukhala ndi matsenga ako,
13 Malangizo onse amene unalandira angokutopetsa basi!
14 Ndithudi, anthuwo ali ngati phesi;
15 Umu ndi mmene adzachitire amatsenga,