1 Beli wagwada pansi, Nebo wawerama;
2 Nyamazo zikuwerama ndi kufuna kugwa ndi milunguyo;
3 Mverani Ine, Inu nyumba ya Yakobo,
4 Mpaka pamene mudzakalambe ndi kumera imvi
5 “Kodi inu mudzandifanizira ndi yani, kapena mufananitsa ndi yani?
6 Anthu ena amakhuthula golide mʼzikwama zawo
7 Amanyamula nʼkumayenda nayo milunguyo pa mapewa awo;
8 “Kumbukirani zimenezi ndipo muchite manyazi,
9 Kumbukirani zinthu zakale zinthu zamakedzana;
10 Ndinaneneratu zakumathero kuchokera pachiyambi pomwe.
11 Ndikuyitana chiwombankhanga kuchokera kummawa.
12 Ndimvereni, inu anthu owuma mtima,
13 Ndikubweretsa pafupi tsiku la chipulumutso changa;