Isaías 46

NYA

1 Beli wagwada pansi, Nebo wawerama;

2 Nyamazo zikuwerama ndi kufuna kugwa ndi milunguyo;

3 Mverani Ine, Inu nyumba ya Yakobo,

4 Mpaka pamene mudzakalambe ndi kumera imvi

5 “Kodi inu mudzandifanizira ndi yani, kapena mufananitsa ndi yani?

6 Anthu ena amakhuthula golide mʼzikwama zawo

7 Amanyamula nʼkumayenda nayo milunguyo pa mapewa awo;

8 “Kumbukirani zimenezi ndipo muchite manyazi,

9 Kumbukirani zinthu zakale zinthu zamakedzana;

10 Ndinaneneratu zakumathero kuchokera pachiyambi pomwe.

11 Ndikuyitana chiwombankhanga kuchokera kummawa.

12 Ndimvereni, inu anthu owuma mtima,

13 Ndikubweretsa pafupi tsiku la chipulumutso changa;

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado