1 Yehova akuyankhula ndi wodzozedwa wake
2 Ine ndidzayenda patsogolo pako,
3 Ndidzakupatsa chuma chobisika mu mdima,
4 Chifukwa cha mtumiki wanga Yakobo,
5 Ine ndine Yehova ndipo palibenso wina;
6 kotero kuti kuchokera kummawa mpaka kumadzulo
7 Ndimalenga kuwala ndi mdima,
8 “Iwe thambo gwetsa mvula kuchokera kumwamba;
9 “Tsoka kwa wokangana ndi mlengi wake,
10 Tsoka kwa wofunsa abambo ake kuti,
11 “Yehova
12 Ndine amene ndinapanga dziko lapansi
13 Ndine amene ndidzawutsa Koresi kuti chilungamo changa chikwaniritsidwe:
14 Yehova akuti,
15 Zoonadi inu muli ndi Mulungu wobisika
16 Onse amene amapanga mafano adzawachititsa manyazi ndi kuwanyozetsa.
17 Koma Yehova adzapulumutsa Israeli
18 Yehova
19 Ine sindinayankhule mwachinsinsi,
20 Yehova akuti, “Sonkhanani pamodzi ndipo mubwere;
21 Fotokozani mlandu wanu,
22 “Tembenukirani kwa Ine kuti mupulumuke,
23 Ndalumbira ndekha,
24 Iwo adzanene kwa Ine kuti,
25 Koma mwa Yehova zidzukulu zonse za Israeli