1 Yehova akuti, “Mvera tsopano, iwe Yakobo, mtumiki wanga,
2 Yehova
3 Pakuti ndidzathira madzi pa nthaka yowuma,
4 Iwo adzakula ngati udzu wothirira bwino
5 Wina adzanena kuti, ‘Ine ndine wa Yehova;’
6 “Yehova Mfumu
7 Ndani nanga angafanane ndi Ine? Muloleni kuti ayankhule.
8 Musanjenjemere, musachite mantha.
9 Onse amene amapanga mafano ngachabe,
10 Ndani amasema mulungu ndi kuwumba fano,
11 Iye pamodzi ndi anzake onse adzawachititsa manyazi;
12 Mmisiri wa zitsulo amatenga chitsulo
13 Mmisiri wa matabwa nayenso amayeza mtengo ndi chingwe
14 Amagwetsa mitengo ya mkungudza,
15 Mitengoyo munthu amachitako nkhuni;
16 Chigawo china cha mtengowo amasonkhera moto
17 Chigawo chotsala amapanga kamulungu, fano lake limenelo;
18 Anthu otere sadziwa kanthu, samvetsa kanthu kalikonse;
19 Palibe amene amayima nʼkulingalira.
20 Munthu wotere ali ngati wodya phulusa, maganizo ake opusa amusocheretsa;
21 Yehova akuti, “Iwe Yakobo, kumbukira zinthu izi
22 Ndachotsa zolakwa zako ngati mitambo,
23 Imbani mwachimwemwe, inu zolengedwa zamlengalenga, pakuti Yehova wachita zimenezi;
24 Yehova Mpulumutsi wanu, amene
25 Ndine amene ndinalepheretsa mipingo ya anthu onyenga,
26 Ndine amene ndimatsimikiza mawu a atumiki ake
27 Ndine amene ndinawuza nyanga yayikulu kuti, ‘Uma’
28 Ndine amene ndinanena kwa Koresi kuti, ‘Iye ndiye mʼbusa wanga,’