Isaías 44

NYA

1 Yehova akuti, “Mvera tsopano, iwe Yakobo, mtumiki wanga,

2 Yehova

3 Pakuti ndidzathira madzi pa nthaka yowuma,

4 Iwo adzakula ngati udzu wothirira bwino

5 Wina adzanena kuti, ‘Ine ndine wa Yehova;’

6 “Yehova Mfumu

7 Ndani nanga angafanane ndi Ine? Muloleni kuti ayankhule.

8 Musanjenjemere, musachite mantha.

9 Onse amene amapanga mafano ngachabe,

10 Ndani amasema mulungu ndi kuwumba fano,

11 Iye pamodzi ndi anzake onse adzawachititsa manyazi;

12 Mmisiri wa zitsulo amatenga chitsulo

13 Mmisiri wa matabwa nayenso amayeza mtengo ndi chingwe

14 Amagwetsa mitengo ya mkungudza,

15 Mitengoyo munthu amachitako nkhuni;

16 Chigawo china cha mtengowo amasonkhera moto

17 Chigawo chotsala amapanga kamulungu, fano lake limenelo;

18 Anthu otere sadziwa kanthu, samvetsa kanthu kalikonse;

19 Palibe amene amayima nʼkulingalira.

20 Munthu wotere ali ngati wodya phulusa, maganizo ake opusa amusocheretsa;

21 Yehova akuti, “Iwe Yakobo, kumbukira zinthu izi

22 Ndachotsa zolakwa zako ngati mitambo,

23 Imbani mwachimwemwe, inu zolengedwa zamlengalenga, pakuti Yehova wachita zimenezi;

24 Yehova Mpulumutsi wanu, amene

25 Ndine amene ndinalepheretsa mipingo ya anthu onyenga,

26 Ndine amene ndimatsimikiza mawu a atumiki ake

27 Ndine amene ndinawuza nyanga yayikulu kuti, ‘Uma’

28 Ndine amene ndinanena kwa Koresi kuti, ‘Iye ndiye mʼbusa wanga,’

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado