Isaías 43

NYA

1 Koma tsopano, Yehova

2 Pamene ukuwoloka nyanja,

3 Chifukwa Ine Yehova, Mulungu wako,

4 Popeza kuti ndiwe wamtengowapatali wolemekezeka ndi wapamtima panga,

5 Usachite mantha, pakuti Ine ndili nawe;

6 Ndidzawuza a kumpoto kuti, ‘Amasuleni,’

7 onsewo amadziwika ndi dzina langa;

8 Tulutsa anthu amene ali nawo maso koma sakupenya,

9 Mitundu yonse ya anthu isonkhane pamodzi,

10 Yehova akunena kuti, “Inu Aisraeli ndinu mboni zanga,

11 Akutero Yehova, “Ine, Inetu ndine Yehova,

12 Ndine amene ndinaneneratu, amene ndinakupulumutsa;

13 “Ine ndine Mulungu kuyambira nthawi yamakedzana, ndipo ndidzakhalabe Mulungu ku nthawi zonse.

14 Yehova akuti,

15 Ine ndine Yehova, Woyera wanu uja,

16 Yehova

17 Iye anasonkhanitsa magaleta, akavalo,

18 “Iwalani zinthu zakale;

19 Taonani, Ine ndikuchita zinthu zatsopano!

20 Nyama zakuthengo, nkhandwe ndi akadzidzi

21 Anthu amene ndinadziwumbira ndekha

22 “Komatu simunapemphera kwa Ine, Inu a mʼbanja la Yakobo,

23 Simunabweretse kwa Ine nkhosa za nsembe zopsereza,

24 Simunandigulire bango lonunkhira

25 “Ine, Inetu, ndi amene ndimafafaniza

26 Mundikumbutse zakale,

27 Kholo lanu loyamba linachimwa;

28 Chifukwa chake Ine ndidzanyazitsa akuluakulu a Nyumba yanu ya mapemphero,

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado