1 Koma tsopano, Yehova
2 Pamene ukuwoloka nyanja,
3 Chifukwa Ine Yehova, Mulungu wako,
4 Popeza kuti ndiwe wamtengowapatali wolemekezeka ndi wapamtima panga,
5 Usachite mantha, pakuti Ine ndili nawe;
6 Ndidzawuza a kumpoto kuti, ‘Amasuleni,’
7 onsewo amadziwika ndi dzina langa;
8 Tulutsa anthu amene ali nawo maso koma sakupenya,
9 Mitundu yonse ya anthu isonkhane pamodzi,
10 Yehova akunena kuti, “Inu Aisraeli ndinu mboni zanga,
11 Akutero Yehova, “Ine, Inetu ndine Yehova,
12 Ndine amene ndinaneneratu, amene ndinakupulumutsa;
13 “Ine ndine Mulungu kuyambira nthawi yamakedzana, ndipo ndidzakhalabe Mulungu ku nthawi zonse.
14 Yehova akuti,
15 Ine ndine Yehova, Woyera wanu uja,
16 Yehova
17 Iye anasonkhanitsa magaleta, akavalo,
18 “Iwalani zinthu zakale;
19 Taonani, Ine ndikuchita zinthu zatsopano!
20 Nyama zakuthengo, nkhandwe ndi akadzidzi
21 Anthu amene ndinadziwumbira ndekha
22 “Komatu simunapemphera kwa Ine, Inu a mʼbanja la Yakobo,
23 Simunabweretse kwa Ine nkhosa za nsembe zopsereza,
24 Simunandigulire bango lonunkhira
25 “Ine, Inetu, ndi amene ndimafafaniza
26 Mundikumbutse zakale,
27 Kholo lanu loyamba linachimwa;
28 Chifukwa chake Ine ndidzanyazitsa akuluakulu a Nyumba yanu ya mapemphero,