1 “Nayu mtumiki wanga, amene ndimamuchirikiza,
2 Iye sadzafuwula, sadzamveka mawu,
3 Bango lophwanyika sadzalithyola,
4 sadzafowoka kapena kukhumudwa
5 Yehova Mulungu
6 “Ine Yehova, ndakuyitana chifukwa Ine ndine wolungama;
7 Udzatsekula maso a anthu osaona,
8 “Ine ndine Yehova: dzina langa ndi limenelo!
9 Taonani, zinthu zimene ndinalosera kale zachitikadi,
10 Imbirani Yehova nyimbo yatsopano,
11 Chipululu ndi mizinda yake zikweze mawu awo;
12 Atamande Yehova
13 Yehova adzapita ku nkhondo ngati munthu wamphamvu,
14 Yehova akuti, “Ndakhala ndili chete kwa nthawi yayitali,
15 Ndidzawononga mapiri ndi zitunda
16 Ndidzatsogolera anthu osaona mʼmisewu imene sanayidziwe,
17 Koma onse amene amadalira mafano
18 “Imvani, agonthi inu;
19 Ali wosaona ndani, si mtumiki wanga kodi?
20 Iwe waona zinthu zambiri, koma sunazisamale;
21 Chinamukomera Yehova
22 Koma awa ndi anthu amene afunkhidwa ndi kuwalanda zinthu zawo,
23 Kodi ndani wa inu amene adzamvetsera zimenezi
24 Ndani anapereka Yakobo kwa ofunkha,
25 Motero anawakwiyira kwambiri,