Isaías 41

NYA

1 “Khalani chete pamaso panga, inu mayiko a mʼmbali mwa nyanja!

2 “Ndani anadzutsa wochokera kummawa

3 Amawalondola namayenda mosavutika,

4 Ndani anachita zimenezi ndi kuzitsiriza,

5 Mayiko amʼmbali mwa nyanja aona zimenezi ndipo akuopa;

6 aliyense akuthandiza mnzake

7 Mʼmisiri wa matabwa amalimbikitsa mʼmisiri wa golide,

8 “Koma Iwe Israeli mtumiki wanga,

9 Ndinakutengani kuchokera ku mapeto a dziko lapansi,

10 Tsono usaope, pakuti Ine ndili nawe;

11 “Onse amene akupsera mtima

12 Udzafunafuna adani ako,

13 Pakuti Ine Yehova, ndine Mulungu wako,

14 Usachite mantha, iwe Yakobo wofowoka ngati nyongolotsi,

15 “Taona, ndidzakusandutsa ngati chipangizo chopunthira tirigu

16 Udzawapeta ndipo adzawuluka ndi mphepo komanso

17 “Pamene amphawi ndi osauka akufunafuna madzi,

18 Ndidzayendetsa mitsinje mʼmalo owuma,

19 Mʼchipululu ndidzameretsa

20 kuti anthu aone ndi kudziwa;

21 “Yehova akuwuza milungu ina kuti, ‘Fotokozani mlandu wanu.’

22 Bwerani ndi milungu yanu kuti idzatiwuze

23 tiwuzeni kuti kutsogolo kuli zotani,

24 Koma inu sindinu kanthu

25 “Ndinawutsa munthu wina kumpoto ndipo anabwera,

26 Ndani anawululiratu zimenezi poyamba pomwe, kuti ife tidziwe,

27 Ine ndinali woyamba kumuwuza Ziyoni kuti, ‘Taona, si awa akubwera apawa!’

28 Koma ndikayangʼana palibe ndi mmodzi yemwe,

29 Taonani, milungu yonseyi ndi yachinyengo!

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado