1 Atonthozeni, atonthozeni anthu anga,
2 Ayankhuleni moleza mtima anthu a ku Yerusalemu
3 Mawu a wofuwula mʼchipululu akuti,
4 Chigwa chilichonse achidzaze.
5 Ndipo ulemerero wa Yehova udzaonekera,
6 Wina ananena kuti, “Lengeza.”
7 Udzu umanyala ndipo maluwa amafota
8 Udzu umanyala ndipo maluwa amafota,
9 Iwe amene ukulengeza nkhani yabwino ku Ziyoni,
10 Taonani, Ambuye Yehova akubwera mwamphamvu,
11 Iye adzasamalira nkhosa zake ngati mʼbusa:
12 Kodi ndani akhoza kuyeza kuchuluka kwa madzi a mʼnyanja ndi chikhatho chake,
13 Ndani anapereka malangizo kwa Mzimu wa Yehova
14 Kodi Yehova anapemphapo nzeru kwa yani kuti akhale wopenya,
15 Ndithudi mitundu ya anthu ili ngati dontho la madzi ochoka mu mtsuko.
16 Nkhalango ya ku Lebanoni singakwanire nkhuni zosonkhera moto pa guwa lansembe,
17 Pamaso pa Yehova mitundu yonse ya anthu ili ngati chinthu chopandapake;
18 Kodi tsono Mulungu mungamuyerekeze ndi yani?
19 Likakhala fano, mʼmisiri ndiye analipanga
20 Mʼmphawi amene sangathe kupeza ngakhale chopereka nsembe chotere
21 Kodi simukudziwa?
22 Yehova amene amakhala pa mpando wake waufumu kumwamba ndiye analenga dziko lapansi,
23 Amatsitsa pansi mafumu amphamvu
24 Inde, iwo ali ngati mbewu zimene zangodzalidwa kumene
25 Woyera uja akuti, “Kodi mudzandiyerekeza Ine ndi yani?
26 Tayangʼanani mlengalenga ndipo onani.
27 Iwe Yakobo, chifukwa chiyani umanena
28 Kodi simukudziwa?
29 Iye amalimbitsa ofowoka
30 Ngakhale achinyamata amalefuka ndi kufowoka,
31 koma iwo amene amakhulupirira Yehova