1 Yehova akuti,
2 Nʼchifukwa chiyani pamene ndinabwera kudzakupulumutsani panalibe munthu?
3 Ndinaphimba thambo ndi mdima
4 Ambuye Yehova anandiphunzitsa mawu oyenera kuyankhula
5 Ambuye Yehova wanditsekula makutu anga,
6 Ndinapereka msana wanga kwa ondimenya
7 Popeza Ambuye Yehova amandithandiza,
8 Wondikhalira kumbuyo ali pafupi,
9 Ambuye Yehova ndiye amene amandithandiza.
10 Ndani mwa inu amaopa Yehova
11 Koma tsopano inu nonse amene mumasonkha moto