Isaías 34

NYA

1 Inu anthu a mitundu yonse, bwerani pafupi kuti mumve:

2 Yehova wayipidwa ndi anthu a mitundu yonse;

3 Anthu awo ophedwa adzatayidwa kunja,

4 Dzuwa, mwezi ndi nyenyezi zidzasungunuka

5 Yehova akuti, “Lupanga langa lakhutiratu magazi kumwamba;

6 Lupanga la Yehova lakhuta magazi,

7 Pamodzi ndi anthuwo zidzaphedwanso njati,

8 Iyi ndi nthawi imene Yehova adzalipsira

9 Madzi a mʼmitsinje ya Edomu adzasanduka phula,

10 Motowo sudzazimitsidwa usiku ndi usana;

11 Mʼdzikomo mudzakhala akabawi ndi anungu;

12 Anthu olemekezeka ake sadzatchedwanso mfumu kumeneko;

13 Minga idzamera mʼnyumba zake zankhondo zotetezedwa,

14 Avumbwe adzakumana ndi afisi,

15 Kadzidzi adzamangako chisa chake nʼkuyikirako mazira,

16 Funafunani mʼbuku la Yehova ndi kuwerenga:

17 Yehova wagawa dziko lawo;

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado