1 Inu anthu a mitundu yonse, bwerani pafupi kuti mumve:
2 Yehova wayipidwa ndi anthu a mitundu yonse;
3 Anthu awo ophedwa adzatayidwa kunja,
4 Dzuwa, mwezi ndi nyenyezi zidzasungunuka
5 Yehova akuti, “Lupanga langa lakhutiratu magazi kumwamba;
6 Lupanga la Yehova lakhuta magazi,
7 Pamodzi ndi anthuwo zidzaphedwanso njati,
8 Iyi ndi nthawi imene Yehova adzalipsira
9 Madzi a mʼmitsinje ya Edomu adzasanduka phula,
10 Motowo sudzazimitsidwa usiku ndi usana;
11 Mʼdzikomo mudzakhala akabawi ndi anungu;
12 Anthu olemekezeka ake sadzatchedwanso mfumu kumeneko;
13 Minga idzamera mʼnyumba zake zankhondo zotetezedwa,
14 Avumbwe adzakumana ndi afisi,
15 Kadzidzi adzamangako chisa chake nʼkuyikirako mazira,
16 Funafunani mʼbuku la Yehova ndi kuwerenga:
17 Yehova wagawa dziko lawo;