Isaías 33

NYA

1 Tsoka kwa iwe, iwe wowonongawe,

2 Inu Yehova, mutikomere mtima ife;

3 Mukatulutsa liwu lanu longa bingu mitundu ya anthu imathawa;

4 Zofunkha za ku nkhondo za mitundu ina Aisraeli adzazisonkhanitsa ngati mmene limachitira dzombe.

5 Yehova wakwezeka kwambiri pakuti amakhala pamwamba pa zonse

6 Iye adzakupatsani mtendere pa nthawi yanu,

7 Taonani, anthu awo amphamvu akulira mofuwula mʼmisewu;

8 Mʼmisewu yayikulu mulibe anthu,

9 Dziko likulira ndipo likunka likutha.

10 Yehova akunena kuti, “Tsopano ndidzadzambatuka

11 Zolingalira zanu nʼzachabechabe

12 Anthu a mitundu ina adzatenthedwa ngati miyala ya njereza;

13 Inu amene muli kutali, imvani zimene ndachita;

14 Mu mzinda wa Ziyoni anthu ochimwa agwidwa ndi mantha;

15 Angathe kuti ndi amene amachita zolungama

16 Munthu wotere ndiye adzakhale pa nsanja,

17 Nthawi imeneyo maso a ana adzaona mfumu ya maonekedwe wokongola

18 Mu mtima mwanu muzidzalingalira zoopsa zinachitika kale zija:

19 Simudzawaonanso anthu odzikuza aja,

20 Taonani Ziyoni, mzinda wa zikondwerero zachipembedzo chathu;

21 Kumeneko Yehova adzaonetsa ulemerero wake

22 Pakuti Yehova ndi woweruza wathu,

23 Zingwe za sitima zapamadzi za adani athu zamasuka,

24 Palibe ndi mmodzi yemwe wokhala mʼZiyoni adzanene kuti, “Ndikudwala”

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado