1 Taonani, kudzakhala mfumu ina imene idzalamulira mwachilungamo,
2 Munthu aliyense adzakhala ngati pothawirapo mphepo
3 Ndipo maso a anthu openya sadzakhalanso otseka,
4 Anthu a mtima wopupuluma adzadziwa ndi kuchita zinthu mofatsa,
5 Chitsiru sichidzatchedwanso munthu waulemu wake
6 Pakuti munthu opusa amayankhula zauchitsiru,
7 Munthu woyipa njira zake ndi zoyipanso,
8 Koma munthu wolemekezeka amalingaliranso kuchita zinthu zabwino,
9 Khalani maso, inu akazi
10 Pakapita chaka ndi masiku pangʼono
11 Nthunthumirani inu okhala mosatekesekanu;
12 Dzigugudeni pachifuwa mwachisoni chifukwa minda yachonde,
13 Mʼdziko la anthu anga
14 Nyumba yaufumu idzasiyidwa,
15 Yehova adzatipatsa mzimu wake,
16 Tsono mʼchipululu mudzakhala chiweruzo cholungama
17 Mtendere udzakhala chipatso chachilungamo;
18 Anthu anga adzakhala mʼmidzi yamtendere,
19 Ngakhale nkhalango idzawonongedwa ndi matalala
20 inutu mudzakhala odalitsika ndithu.