1 Tsoka kwa amene amapita ku Igupto kukapempha chithandizo,
2 Komatu Yehovayo ndi wanzeru ndipo angathe kuwononga,
3 Aigupto ndi anthu chabe osati Mulungu;
4 Zimene Yehova akunena kwa ine ndi izi:
5 Monga mbalame zowuluka pamwamba pa zisa zake,
6 Inu Aisraeli, bwererani kwa Iye amene munamuwukira kwakukulu.
7 Pakuti tsiku limenelo nonsenu mudzataya mafano anu a siliva ndi golide amene mumapanga ndi manja anu auchimo.
8 “Aasiriya adzaphedwa ku nkhondo ndi mphamvu osati za munthu.
9 Mfumu yawo idzamwalira ndi mantha,