Isaías 30

NYA

1 Yehova akuti, “Tsoka kwa ana ondipandukira

2 Amapita ku Igupto kukapempha thandizo

3 Koma chitetezo cha Farao chidzakhala manyazi anu,

4 Ngakhale kuti nduna zawo zili ku Zowani,

5 aliyense wa ku Yuda adzachita manyazi

6 Uthenga wonena za nyama za ku Negevi:

7 Amapita ku Igupto amene thandizo lake ndi lachabechabe.

8 Yehova anandiwuza kuti, “Tsopano pita,

9 Amenewa ndi anthu owukira, onama ndi

10 Iwo amawuza alosi kuti,

11 Patukani pa njira ya Yehova,

12 Nʼchifukwa chake Woyerayo wa Israeli akunena kuti,

13 choncho tchimo linalo lidzakhala ngati mingʼalu

14 Lidzaphwanyika ngati mbiya

15 Zimene Ambuye Yehova, Woyerayo wa Israeli ananena ndi izi:

16 Inu mukuti, ‘Ayi ife tidzathawa,

17 Anthu 1,000 mwa inu adzathawa

18 Komatu Yehova akufunitsitsa kuti akukomereni mtima,

19 Inu anthu a ku Ziyoni, amene mukhala mu Yerusalemu simudzaliranso. Mulungu adzakukomerani mtima pamene adzamva kulira kwanu kopempha thandizo! Ndipo akadzamva, adzakuyankhani.

20 Ngakhale Ambuye adzakulowetseni mʼmasautso, aphunzitsi anu sadzakhala kakasi; inu mudzawaona ndi maso anuwo.

21 Ngati mudzapatukira kumanja kapena kumanzere, mudzamva mawu kumbuyo kwanu woti, “Njira ndi iyi; yendani mʼmenemo.”

22 Pamenepo mudzawononga mafano anu okutidwa ndi siliva ndiponso zifanizo zanu zokutidwa ndi golide; mudzawataya ngati zinthu zonyansa ndipo mudzati, “Zichoke zonsezi!”

23 Yehova adzakugwetseraninso mvula pa mbewu zanu zimene mukadzale mʼnthaka, ndipo chakudya chimene mudzakolole chidzakhala chabwino ndi chochuluka. Tsiku limenelo ngʼombe zanu zidzadya msipu wochuluka.

24 Ngʼombe ndi abulu amene amalima mʼmunda adzadya chakudya chamchere, chopetedwa ndi foloko ndi fosholo.

25 Pa tsiku limene adani anu adzaphedwa ndi nsanja zawo kugwa, mitsinje ya madzi idzayenda pa phiri lililonse lalikulu ndi pa phiri lililonse lalingʼono.

26 Mwezi udzawala ngati dzuwa, ndipo kuwala kwa dzuwa kudzawonjezereka kasanu nʼkawiri, ngati kuwala kwa tsiku limodzi. Yehova adzamanga mabala a anthu ake ndi kupoletsa zilonda zimene Iye anachititsa polanga anthu ake.

27 Taonani, Yehova akubwera kuchokera kutali,

28 Mpweya wake uli ngati mtsinje wosefukira,

29 Ndipo inu mudzayimba

30 Anthu adzamva liwu la ulemerero la Yehova

31 Asiriya adzaopa liwu la Yehova,

32 Yehova akamadzalanga adani ake ndi ndodo,

33 Malo otenthera zinthu akonzedwa kale;

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado