1 Tsoka kwa iwe, Arieli, Arieli,
2 Komatu Ine ndidzathira nkhondo Arieli
3 Ine ndidzamanga misasa ya nkhondo kulimbana ndi mzindawo;
4 Utagwetsedwa pansi, iwe udzayankhula kuchokera mʼnthaka,
5 Koma chigulu cha adani ako chidzasanduka chifwirimbwiti.
6 Yehova Wamphamvuzonse adzabwera
7 Tsono chigulu chankhondo cha mitundu ina yonse chimene chikulimbana ndi mzinda wa Arieli
8 Chidzakhala ngati munthu wanjala wolota akudya,
9 Pitirizani kuledzera ndipo mudzakhala opusa.
10 Yehova wakugonetsani tulo tofa nato.
11 Kwa inu mawu onsewa ali ngati buku lotsekedwa, ndipo ngati lipatsidwa kwa wina wodziwa kuwerenga ndi kunena kuti, “Chonde tawerengani bukuli,” iye adzati, “Sindingathe popeza ndi lomatidwa.”
12 Kapena ngati lipatsidwa kwa amene sadziwa kuwerenga ndi kunena kuti, “Chonde werenga bukuli,” iye adzayankha kuti, “Ine sindidziwa kuwerenga.”
13 Ambuye akuti,
14 Nʼchifukwa chakenso Ine ndidzapitirira
15 Tsoka kwa amene amayesetsa
16 Inu mumazondotsa zinthu
17 Kodi Lebanoni posachedwapa sadzasanduka munda wachonde,
18 Tsiku limenelo anthu osamva adzamva mawu a mʼbuku,
19 Anthu odzichepetsa adzakhalanso ndi chimwemwe mwa Yehova;
20 Koma anthu ankhanza adzazimirira,
21 Yehova adzalanga amene amasinjirira munthu kuti apezeke wolakwa,
22 Choncho Yehova amene anawombola Abrahamu, akunena kwa zidzukulu za Yakobo kuti,
23 Akadzaona ana awo ndi
24 Anthu opusa adzapeza nzeru;