Isaías 28

NYA

1 Tsoka ufumu wonyada wa zidakwa za ku Efereimu.

2 Taonani, ambuye ali naye wina wamphamvu ndi nyonga.

3 Ulamuliro wa atsogoleri oledzera

4 Ndipo ulemerero wokongola wa mzinda umene uli ngati duwa

5 Tsiku limenelo Yehova Wamphamvuzonse

6 Iye adzapereka mtima

7 Nawonso awa ali dzandidzandi chifukwa cha vinyo

8 Pa matebulo onse pali masanzi okhaokha

9 Iwo akuti, “Kodi munthu ameneyu akufuna aphunzitse ndani?

10 Akuyesa kumatiphunzitsa pangʼonopangʼono

11 Mulungu adzayankhula kwa anthu ake kudzera mwa anthu aziyankhulo zachilendo, ziyankhulo zosamveka bwino.

12 anakuwuzani kuti,

13 Choncho Yehova adzakuphunzitsani

14 Nʼchifukwa chake imvani mawu a Yehova,

15 Inu mumayankhula monyada kuti, “Ife tinachita pangano ndi imfa,

16 Tsono zimene Ambuye Yehova akunena ndi izi:

17 Ntchito zolungama zidzakhala ngati chingwe choyezera maziko ake,

18 Pangano limene munachita ndi imfa lidzathetsedwa;

19 Ndipo ukadzangofika udzakutengani.

20 Mudzakhala ngati munthu wogona pa bedi lalifupi kwambiri kuti sangathe kutambalitsapo miyendo;

21 Yehova adzamenya nkhondo monga anachitira ku phiri la Perazimu

22 Tsopano lekani kunyoza,

23 Tcherani khutu ndipo mumve mawu anga;

24 Kodi mlimi wofuna kudzala mbewu amangokhalira kutipula kokhakokha?

25 Pamene iye wasalaza mundawo,

26 Mulungu wake amamulangiza

27 Mawere sapunthira chopunthira cha galeta lopanda mikombero,

28 Tirigu ayenera kusinjidwa kuti apangire buledi,

29 Izinso zimachokera kwa Yehova Wamphamvuzonse,

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado