Isaías 35

NYA

1 Chipululu ndi dziko lopanda madzi zidzasangalala;

2 Dzikolo lidzakhala ndi maluwa ochuluka

3 Limbitsani manja ofowoka,

4 nenani kwa a mitima yamantha kuti;

5 Pamenepo maso a anthu osaona adzapenyanso

6 Anthu olumala adzalumpha ngati mbawala,

7 mchenga wotentha udzasanduka dziwe,

8 Ndipo kumeneko kudzakhala msewu waukulu;

9 Kumeneko sikudzakhala mkango,

10 Iwo amene Yehova anawawombola adzabwerera.

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado