1 Chipululu ndi dziko lopanda madzi zidzasangalala;
2 Dzikolo lidzakhala ndi maluwa ochuluka
3 Limbitsani manja ofowoka,
4 nenani kwa a mitima yamantha kuti;
5 Pamenepo maso a anthu osaona adzapenyanso
6 Anthu olumala adzalumpha ngati mbawala,
7 mchenga wotentha udzasanduka dziwe,
8 Ndipo kumeneko kudzakhala msewu waukulu;
9 Kumeneko sikudzakhala mkango,
10 Iwo amene Yehova anawawombola adzabwerera.