Isaías 25

NYA

1 Yehova ndinu Mulungu wanga;

2 Inu mwasandutsa mzinda uja kukhala mulu wamiyala.

3 Nʼchifukwa chake anthu amphamvu adzakulemekezani;

4 Inu mwakhala ngati populumukira pa anthu osauka,

5 ndiponso ngati kutentha mʼdziko lowuma.

6 Pa phiri ili Yehova Wamphamvuzonse adzakonzera

7 Iye adzachotsa kulira

8 Yehova adzathetsa imfa mpaka muyaya,

9 Tsiku limenelo iwo adzati,

10 Yehova adzateteza phiri limeneli ndi dzanja lake;

11 Amowabuwo adzatambasula manja awo mʼmenemo,

12 Iye adzagumula malinga awo ataliatali

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado