Isaías 24

NYA

1 Taonani, Yehova adzawononga dziko lapansi

2 Aliyense zidzamuchitikira mofanana:

3 Dziko lapansi lidzawonongedwa kwathunthu

4 Dziko lapansi likulira ndipo likufota,

5 Anthu ayipitsa dziko lapansi;

6 Nʼchifukwa chake matemberero akuwononga dziko lapansi;

7 Vinyo watsopano watha ndipo mphesa zikufota;

8 Kulira kokometsera kwa matambolini kwatha,

9 Anthu sadzayimbanso akumwa vinyo;

10 Mzinda wachisokonezo uja wawonongeka;

11 Anthu akulira mʼmisewu kufuna vinyo;

12 Mzinda wasanduka bwinja

13 Zimenezi ndizo zidzachitikire mitundu yonse ya dziko lapansi

14 Koma otsala onse akufuwula ndi kuyimba mwachimwemwe;

15 Nʼchifukwa chake inu akummawa, tamandani Yehova;

16 Kuchokera kumalekezero a dziko lapansi tikumva kuyimba kotamanda

17 Inu anthu adziko lapansi, zoopsa, dzenje

18 Aliyense wothawa phokoso la zoopsa

19 Dziko lapansi lathyokathyoka,

20 Dziko lapansi likudzandira ngati munthu woledzera

21 Tsiku limenelo Yehova adzalanga

22 Mulungu adzawasonkhanitsa pamodzi

23 Mwezi udzanyazitsidwa, dzuwa lidzachita manyazi;

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado