1 Taonani, Yehova adzawononga dziko lapansi
2 Aliyense zidzamuchitikira mofanana:
3 Dziko lapansi lidzawonongedwa kwathunthu
4 Dziko lapansi likulira ndipo likufota,
5 Anthu ayipitsa dziko lapansi;
6 Nʼchifukwa chake matemberero akuwononga dziko lapansi;
7 Vinyo watsopano watha ndipo mphesa zikufota;
8 Kulira kokometsera kwa matambolini kwatha,
9 Anthu sadzayimbanso akumwa vinyo;
10 Mzinda wachisokonezo uja wawonongeka;
11 Anthu akulira mʼmisewu kufuna vinyo;
12 Mzinda wasanduka bwinja
13 Zimenezi ndizo zidzachitikire mitundu yonse ya dziko lapansi
14 Koma otsala onse akufuwula ndi kuyimba mwachimwemwe;
15 Nʼchifukwa chake inu akummawa, tamandani Yehova;
16 Kuchokera kumalekezero a dziko lapansi tikumva kuyimba kotamanda
17 Inu anthu adziko lapansi, zoopsa, dzenje
18 Aliyense wothawa phokoso la zoopsa
19 Dziko lapansi lathyokathyoka,
20 Dziko lapansi likudzandira ngati munthu woledzera
21 Tsiku limenelo Yehova adzalanga
22 Mulungu adzawasonkhanitsa pamodzi
23 Mwezi udzanyazitsidwa, dzuwa lidzachita manyazi;