Isaías 26

NYA

1 Tsiku limenelo anthu a mʼdziko la Yuda adzayimba nyimbo iyi.

2 Tsekulani zipata za mzinda

3 Inu mudzamupatsa munthu

4 Mudalireni Yehova mpaka muyaya,

5 Iye amatsitsa anthu amene amadziyika pamwamba,

6 Mapazi a anthu akuwupondereza,

7 Njira ya munthu wolungama ndi yosalaza,

8 Inde Yehova, timayenda mʼnjira zanu zolungama,

9 Moyo wanga umalakalaka Inu usiku wonse;

10 Ngakhale mukomere mtima anthu oyipa,

11 Inu Yehova, mwatukula dzanja lanu kuti muwalange,

12 Yehova, mumatipatsa mtendere;

13 Inu Yehova Mulungu wathu, ngakhale takhala tikulamulidwa ndi ena mʼmalo mwanu,

14 Iwo tsopano sadzadzukanso;

15 Inu Yehova, mwaukulitsa mtundu wathu;

16 Yehova, anthu anu anabwera kwa Inu pamene anali mʼmasautso;

17 Monga mayi woyembekezera pamene nthawi yake yobereka yayandikira

18 Ife chimodzimodzi tinamva ululu, ngati mayi pa nthawi yobala mwana,

19 Koma anthu anu amene anafa adzakhalanso ndi moyo;

20 Abale anga, pitani mukalowe mʼnyumba zanu

21 Taonani, Yehova akubwera kuchokera kumene amakhala;

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado