1 Tsiku limenelo anthu a mʼdziko la Yuda adzayimba nyimbo iyi.
2 Tsekulani zipata za mzinda
3 Inu mudzamupatsa munthu
4 Mudalireni Yehova mpaka muyaya,
5 Iye amatsitsa anthu amene amadziyika pamwamba,
6 Mapazi a anthu akuwupondereza,
7 Njira ya munthu wolungama ndi yosalaza,
8 Inde Yehova, timayenda mʼnjira zanu zolungama,
9 Moyo wanga umalakalaka Inu usiku wonse;
10 Ngakhale mukomere mtima anthu oyipa,
11 Inu Yehova, mwatukula dzanja lanu kuti muwalange,
12 Yehova, mumatipatsa mtendere;
13 Inu Yehova Mulungu wathu, ngakhale takhala tikulamulidwa ndi ena mʼmalo mwanu,
14 Iwo tsopano sadzadzukanso;
15 Inu Yehova, mwaukulitsa mtundu wathu;
16 Yehova, anthu anu anabwera kwa Inu pamene anali mʼmasautso;
17 Monga mayi woyembekezera pamene nthawi yake yobereka yayandikira
18 Ife chimodzimodzi tinamva ululu, ngati mayi pa nthawi yobala mwana,
19 Koma anthu anu amene anafa adzakhalanso ndi moyo;
20 Abale anga, pitani mukalowe mʼnyumba zanu
21 Taonani, Yehova akubwera kuchokera kumene amakhala;