1 Nazi zinthu zokhudza Yuda ndi Yerusalemu, zimene Yesaya mwana wa Amozi anaziona mʼmasomphenya:
2 Mʼmasiku otsiriza,
3 Anthu ambiri adzabwera ndikunena kuti,
4 Iye adzaweruza pakati pa mayiko,
5 Inu nyumba ya Yakobo, bwerani,
6 Inu Yehova mwawakana anthu anu,
7 Dziko lawo ndi lodzaza ndi siliva ndi golide;
8 Dziko lawo ndi lodzaza ndi mafano;
9 Tsono munthu aliyense adzachepetsedwa
10 Lowani mʼmatanthwe,
11 Kudzikuza kwa anthu kudzatha,
12 Yehova Wamphamvuzonse wakonzeratu tsiku
13 tsiku la mikungudza yonse ya ku Lebanoni, yayitali ndi yoonekera patali,
14 tsiku la mapiri onse ataliatali
15 tsiku la nsanja zonse zazitali
16 tsiku la sitima zapamadzi zonse za ku Tarisisi
17 Kudzikuza kwa munthu kudzatha
18 ndipo mafano onse adzatheratu.
19 Anthu adzathawira mʼmapanga a matanthwe
20 Tsiku limenelo anthu adzatayira
21 Adzathawira mʼmapanga a matanthwe
22 Lekani kudalira munthu,