Isaías 2

NYA

1 Nazi zinthu zokhudza Yuda ndi Yerusalemu, zimene Yesaya mwana wa Amozi anaziona mʼmasomphenya:

2 Mʼmasiku otsiriza,

3 Anthu ambiri adzabwera ndikunena kuti,

4 Iye adzaweruza pakati pa mayiko,

5 Inu nyumba ya Yakobo, bwerani,

6 Inu Yehova mwawakana anthu anu,

7 Dziko lawo ndi lodzaza ndi siliva ndi golide;

8 Dziko lawo ndi lodzaza ndi mafano;

9 Tsono munthu aliyense adzachepetsedwa

10 Lowani mʼmatanthwe,

11 Kudzikuza kwa anthu kudzatha,

12 Yehova Wamphamvuzonse wakonzeratu tsiku

13 tsiku la mikungudza yonse ya ku Lebanoni, yayitali ndi yoonekera patali,

14 tsiku la mapiri onse ataliatali

15 tsiku la nsanja zonse zazitali

16 tsiku la sitima zapamadzi zonse za ku Tarisisi

17 Kudzikuza kwa munthu kudzatha

18 ndipo mafano onse adzatheratu.

19 Anthu adzathawira mʼmapanga a matanthwe

20 Tsiku limenelo anthu adzatayira

21 Adzathawira mʼmapanga a matanthwe

22 Lekani kudalira munthu,

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado