1 Masomphenya wonena za Yuda ndi Yerusalemu, amene Yesaya mwana wa Amozi, anaona pa nthawi ya ulamuliro wa Uziya, Yotamu, Ahazi ndi Hezekiya, mafumu a Yuda.
2 Tamverani, miyamba inu! Tchera khutu, iwe dziko lapansi!
3 Ngʼombe imadziwa mwini wake,
4 Haa, mtundu wochimwa,
5 Chifukwa chiyani mukufuna kuti muzingolangidwabe?
6 Kuchokera ku phazi mpaka ku mutu
7 Dziko lanu lasanduka bwinja,
8 Mwana wamkazi wa Ziyoni watsala yekha
9 Yehova Wamphamvuzonse akanapanda
10 Imvani mawu a Yehova,
11 Yehova akuti, “Kodi ndili nazo chiyani
12 Ndani anakulamulirani kuti
13 Siyani kubweretsa nsembe zachabechabezo!
14 Zikondwerero zanu za Mwezi Watsopano ndi masiku anu opatulika
15 Mukamatambasula manja anu popemphera,
16 sambani, dziyeretseni.
17 phunzirani kuchita zabwino!
18 Yehova akuti,
19 Ngati muli okonzeka kundimvera
20 koma mukakana ndi kuwukira
21 Taonani momwe mzinda wokhulupirika
22 Siliva wako wasanduka wachabechabe,
23 Atsogoleri ako ndi owukira,
24 Nʼchifukwa chake Ambuye Yehova Wamphamvu,
25 Ndidzatambasula dzanja langa kuti ndilimbane nawe;
26 Ndidzabwezeretsa oweruza ako ngati masiku amakedzana,
27 Ziyoni adzawomboledwa mwa chiweruzo cholungama,
28 Koma owukira ndi ochimwa adzawawonongera pamodzi,
29 “Mudzachita nayo manyazi mitengo ya thundu
30 Mudzakhala ngati mtengo wa thundu umene masamba ake akufota,
31 Munthu wamphamvu adzasanduka ngati udzu wowuma,