Isaías 3

NYA

1 Taonani tsopano, Ambuye

2 anthu amphamvu ndi asilikali ankhondo,

3 atsogoleri a ankhondo makumi asanu ndi anthu olemekezeka,

4 Ndidzawayikira anyamata kuti akhale mafumu awo;

5 Anthu adzazunzana,

6 Munthu adzagwira mʼbale wake

7 Koma tsiku limenelo mʼbale wakeyo adzafuwula kuti,

8 Yerusalemu akudzandira,

9 Maonekedwe a nkhope zawo amawatsutsa;

10 Nena kwa olungama kuti zonse zidzawayendera bwino,

11 Tsoka kwa anthu oyipa! Mavuto ali pa iwo!

12 Achinyamata akupondereza anthu anga,

13 Yehova wakhala pamalo pake mʼbwalo la milandu;

14 Yehova akuwazenga milandu

15 Nʼchifukwa chiyani inu mukupsinja anthu anga,

16 Yehova akunena kuti,

17 Nʼchifukwa chake Ambuye, adzatulutsa zipere pa mitu ya akazi a ku Ziyoniwo;

18 Tsiku limenelo Ambuye adzawachotsera zodzikongoletsera zawo: za mʼmiyendo, za ku mutu za mʼkhosi,

19 ndolo ndi zibangiri, nsalu zophimba pa nkhope,

20 maduku, zigwinjiri za mʼmiyendo ndi malamba, mabotolo a zonunkhira ndi zithumwa,

21 mphete ndi zipini,

22 zovala za pa mphwando, zipewa ndi mwinjiro, zikwama,

23 magalasi oyangʼanira, zovala zosalala, nduwira ndiponso nsalu za mʼmapewa.

24 Mʼmalo mwa kununkhira azidzanunkha,

25 Iwe Yerusalemu anthu ako aamuna adzaphedwa ndi lupanga,

26 Pa zipata za Ziyoni padzakhala kubuma ndi kulira;

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado