Isaías 17

NYA

1 Uthenga wonena za Damasiko:

2 Mizinda ya Aroeri idzakhala yopanda anthu

3 Ku Efereimu sikudzakhalanso linga,

4 “Tsiku limenelo ulemerero wa Yakobo udzazimirira;

5 Israeli adzakhala ngati munda wa tirigu

6 Komabe Aisraeli ochepa okha ndiwo ati adzatsale

7 Tsiku limenelo anthu adzayangʼana Mlengi wawo

8 Iwo sadzakhulupiriranso maguwa ansembe,

9 Tsiku limenelo mizinda yawo yamphamvu, imene anasiya chifukwa cha Aisraeli, idzakhala ngati malo osiyidwa kuti awirire ndi kumera ziyangoyango. Ndipo yonse idzakhala mabwinja.

10 Inu mwayiwalatu Mulungu Mpulumutsi wanu;

11 nimuyembekeza kuti zikule tsiku lomwelo

12 Aa, mkokomo wa anthu a mitundu yambiri,

13 Ngakhale ankhondo a mitundu ina akubwera ndi mkokomo ngati wa madzi ambiri,

14 Pofika nthawi yamadzulo zoopsa zidzayamba kuchitika,

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado