1 Uthenga wonena za Damasiko:
2 Mizinda ya Aroeri idzakhala yopanda anthu
3 Ku Efereimu sikudzakhalanso linga,
4 “Tsiku limenelo ulemerero wa Yakobo udzazimirira;
5 Israeli adzakhala ngati munda wa tirigu
6 Komabe Aisraeli ochepa okha ndiwo ati adzatsale
7 Tsiku limenelo anthu adzayangʼana Mlengi wawo
8 Iwo sadzakhulupiriranso maguwa ansembe,
9 Tsiku limenelo mizinda yawo yamphamvu, imene anasiya chifukwa cha Aisraeli, idzakhala ngati malo osiyidwa kuti awirire ndi kumera ziyangoyango. Ndipo yonse idzakhala mabwinja.
10 Inu mwayiwalatu Mulungu Mpulumutsi wanu;
11 nimuyembekeza kuti zikule tsiku lomwelo
12 Aa, mkokomo wa anthu a mitundu yambiri,
13 Ngakhale ankhondo a mitundu ina akubwera ndi mkokomo ngati wa madzi ambiri,
14 Pofika nthawi yamadzulo zoopsa zidzayamba kuchitika,