Isaías 18

NYA

1 Tsoka kwa anthu a ku Kusi.

2 Dziko limenelo limatumiza akazembe pa mtsinje wa Nailo,

3 Inu nonse anthu a pa dziko lonse,

4 Pakuti Yehova akunena kwa ine kuti,

5 Pakuti, anthu asanayambe kukolola, maluwa atayoyoka

6 Mitembo ya anthu ankhondo adzasiyira mbalame zamʼmapiri zodya nyama

7 Pa nthawi imeneyo anthu adzabwera ndi mphatso kwa Yehova Wamphamvuzonse,

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado