1 Tsoka kwa anthu a ku Kusi.
2 Dziko limenelo limatumiza akazembe pa mtsinje wa Nailo,
3 Inu nonse anthu a pa dziko lonse,
4 Pakuti Yehova akunena kwa ine kuti,
5 Pakuti, anthu asanayambe kukolola, maluwa atayoyoka
6 Mitembo ya anthu ankhondo adzasiyira mbalame zamʼmapiri zodya nyama
7 Pa nthawi imeneyo anthu adzabwera ndi mphatso kwa Yehova Wamphamvuzonse,