Isaías 16

NYA

1 Anthu a ku Mowabu

2 Monga momwe mbalame zimawulukira uku ndi uku

3 Amowabu aja anawuza a ku Yuda kuti,

4 Lolani kuti anthu othawa nkhondo a ku Mowabu azikhala pakati panu;

5 Mpando waufumu udzakhazikitsidwa mwachikondi;

6 Tinamva kuti Mowabu anadzikuza kwambiri.

7 Nʼchifukwa chake Amowabu akulira kwambiri;

8 Minda ya ku Hesiboni yauma,

9 Kotero Ine ndikulira, monga mmene akulirira anthu a ku Yazeri,

10 Chimwemwe ndi chisangalalo zalekeka ku minda yanu ya zipatso;

11 Chifukwa chake moyo wanga ukulira ngati pangwe kulirira Mowabu,

12 Ngakhale anthu a ku Mowabu

13 Awa ndi mawu amene Yehova wayankhula kale zokhudza Mowabu.

14 Koma tsopano Yehova akuti, “Zisanathe zaka zitatu, potsata mʼmene munthu waganyu amawerengera, ulemerero wa Mowabu udzakhala utatheratu ndipo anthu ake ambiri adzakhala atawonongeka, ndipo opulumuka ake adzakhala ochepa ndi ofowoka.”

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado