1 Uthenga wonena za Mowabu:
2 Anthu a ku Diboni akupita ku nyumba ya milungu yawo,
3 Mʼmisewu akuvala ziguduli;
4 Anthu a ku Hesiboni ndi Eleali akulira mofuwula,
5 Inenso ndikulirira Mowabu;
6 Madzi a ku Nimurimu aphwa
7 Kotero kuti chuma chomwe anachipeza ndi kuchisunga,
8 Kulira kwawo kukumveka mʼdziko lonse la Mowabu;
9 Madzi a ku Dimoni afiira ndi magazi,