1 Yehova adzachitira chifundo Yakobo;
2 Anthu a mitundu ina adzaperekeza a Israeli
3 Yehova akadzakupumitsani ku zowawa ndi mavuto, ndiponso kuntchito yakalavulagaga imene ankakugwiritsani,
4 mudzayankhula monyogodola mfumu ya Babuloni kuti,
5 Yehova wathyola chikwapu cha anthu oyipa,
6 Mfumu ya ku Babuloni inkakantha mitundu ya anthu mwaukali
7 Koma tsopano mayiko onse ali pa mpumulo ndi pa mtendere;
8 Ngakhale mitengo ya payini ndi mikungudza ya ku Lebanoni
9 Ku manda kwatekeseka
10 Onse adzayankha;
11 Ulemerero wako wonse walowa mʼmanda,
12 Wagwa pansi bwanji kuchoka kumwamba,
13 Mu mtima mwako unkanena kuti,
14 Ndidzakwera pamwamba pa mitambo;
15 Koma watsitsidwa mʼmanda
16 Anthu akufa adzakupenyetsetsa
17 munthu amene anasandutsa dziko lonse chipululu,
18 Mafumu onse a mitundu ya anthu akugona mwaulemu
19 Koma iwe watayidwa kunja kwa manda ako,
20 Sudzayikidwa nawo mʼmanda mwaulemu,
21 Konzani malo woti muphere ana ake aamuna
22 Yehova Wamphamvuzonse akuti,
23 “Ndidzawusandutsa mzindawo malo okhalamo anungu
24 Yehova Wamphamvuzonse walumbira kuti,
25 Ndidzawawononga Asiriya mʼdziko langa;
26 Izi ndizo ndakonza kuti zichitike pa dziko lonse lapansi,
27 Pakuti Yehova Wamphamvuzonse watsimikiza, ndipo ndani angamuletse?
28 Uthenga uwu unabwera chaka chimene mfumu Ahazi anamwalira:
29 Musakondwere inu Afilisti nonse
30 Osaukitsitsa adzapeza chakudya
31 Lirani kwambiri, anthu a pa chipata! Fuwulani kwambiri, anthu a mu mzinda!
32 Kodi tidzawayankha chiyani