1 Uthenga onena za Babuloni umene Yesaya mwana wa Amozi anawulandira:
2 Kwezani mbendera yankhondo pa phiri loti see,
3 Ine Yehova, ndalamulira ankhondo anga;
4 Tamvani phokoso ku mapiri,
5 Iwo akuchokera ku mayiko akutali,
6 Lirani mofuwula, pakuti tsiku la Yehova layandikira;
7 Zimenezi zinafowoketsa manja onse,
8 Anthu adzagwidwa ndi mantha aakulu,
9 Taonani, tsiku la Yehova likubwera,
10 Nyenyezi zakumwamba ndiponso zonse zamlengalenga
11 Ndidzalanga dziko lonse chifukwa cha zolakwa zake,
12 Ndidzasandutsa anthu kukhala ovuta kupeza kuposa mmene amasowera golide wabwino.
13 Tsono ndidzagwedeza miyamba
14 Ngati mbawala zosakidwa,
15 Aliyense amene atadzapezeke ndi kugwidwa
16 Ana awo akhanda adzaphwanyidwa iwo akuona;
17 Taona, Ine ndidzadzutsa Amedi amene safuna siliva
18 Adzapha anyamata ndi mauta awo;
19 Babuloni, ufumu wake ndi waulemerero kuposa mafumu onse.
20 Anthu sadzakhalamonso
21 Koma nyama zakuthengo ndizo zidzakhale kumeneko,
22 Mu nsanja zake muzidzalira afisi,