1 Tsiku limenelo aliyense wa inu adzati:
2 Zoonadi, Mulungu ndiye Mpulumutsi wanga;
3 Mudzakondwera popeza Yehova
4 Tsiku limenelo mudzati:
5 Imbirani Yehova, pakuti wachita ntchito zazikulu;
6 Fuwulani ndi kuyimba mwachimwemwe, inu anthu a ku Ziyoni;