Isaías 11

NYA

1 Padzatuluka mphukira pa tsinde la Yese

2 Mzimu wa Yehova udzakhala pa iye

3 Ndipo kuopa Yehova ndiye chidzakhale chinthu chomukondweretsa.

4 koma amphawi adzawaweruza mwachilungamo,

5 Chilungamo chidzakhala ngati lamba wake

6 Mʼmbulu udzakhala pamodzi ndi mwana wankhosa,

7 Ngʼombe yayikazi ndi chimbalangondo zidzadya pamodzi,

8 Mwana wakhanda adzasewera pa dzenje la mamba,

9 Sipadzakhala chilichonse chopweteka kapena chowononga

10 Tsiku limenelo mfumu yatsopano yochokera pa Muzu wa Yese idzakhala ngati chizindikiro kwa anthu a mitundu yonse. Mitundu ya anthu idzasonkhana kwa Iye, ndipo malo awo okhalapo adzakhala aulemerero.

11 Tsiku limenelo Ambuye adzatambasula dzanja lake kachiwiri kuti awombole anthu ake otsalira ku Asiriya, ku Igupto, ku Patirosi, Kusi, ku Elamu, ku Sinana, ku Hamati ndi pa zilumba za nyanja yamchere.

12 Adzakwezera mitundu ya anthu mbendera,

13 Nsanje ya Efereimu idzatha,

14 Yuda ndi Efereimu adzathira nkhondo pa Afilisti mbali ya kumadzulo;

15 Yehova adzaphwetsa

16 Padzakhala msewu waukulu woti ayendepo anthu ake otsalira

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado