Eclesiastes 11

NYA

1 Ponya chakudya chako pa madzi,

2 Ndalama zako uzisungitse kwa anthu asanu ndi awiri, inde kwa anthu asanu ndi atatu,

3 Ngati mitambo yadzaza ndi madzi,

4 Amene amayangʼana mphepo sadzadzala;

5 Momwe sudziwira mayendedwe a mphepo,

6 Dzala mbewu zako mmawa

7 Kuwala nʼkwabwino,

8 Munthu akakhala wa zaka zambiri,

9 Kondwera mnyamata iwe, pamene ukanali wamngʼono,

10 Choncho uchotse zokusautsa mu mtima mwako,

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado