1 Ponya chakudya chako pa madzi,
2 Ndalama zako uzisungitse kwa anthu asanu ndi awiri, inde kwa anthu asanu ndi atatu,
3 Ngati mitambo yadzaza ndi madzi,
4 Amene amayangʼana mphepo sadzadzala;
5 Momwe sudziwira mayendedwe a mphepo,
6 Dzala mbewu zako mmawa
7 Kuwala nʼkwabwino,
8 Munthu akakhala wa zaka zambiri,
9 Kondwera mnyamata iwe, pamene ukanali wamngʼono,
10 Choncho uchotse zokusautsa mu mtima mwako,