Eclesiastes 10

NYA

1 Monga ntchentche zakufa zimayika fungo loyipa mʼmafuta onunkhira,

2 Mtima wa munthu wanzeru umamutsogolera bwino,

3 Chitsiru ngakhale chikamayenda mu msewu,

4 Ngati wolamulira akukwiyira,

5 Pali choyipa chimene ndinachiona pansi pano,

6 Zitsiru amazipatsa ntchito zambiri zapamwamba,

7 Ndaona akapolo atakwera pa akavalo,

8 Amene amakumba dzenje adzagwamo yekha;

9 Amene amaphwanya miyala adzapwetekedwa ndi miyalayo;

10 Ngati nkhwangwa ili yobuntha

11 Nʼkopanda phindu kudziwa kuseweretsa njoka

12 Mawu a pakamwa pa munthu wanzeru ndi okondweretsa,

13 Chitsiru chimayamba ndi mawu opusa;

14 ndipo chitsiru chimachulukitsa mawu.

15 Chitsiru chimatopa msanga ndi ntchito yochepa;

16 Tsoka kwa iwe, iwe dziko ngati mfumu yako ikali mwana,

17 Wodala iwe, iwe dziko ngati mfumu yako ndi mwana wolemekezeka

18 Ngati munthu ndi waulesi, denga lake limaloshoka;

19 Phwando ndi lokondweretsa anthu,

20 Usanyoze mfumu ngakhale mu mtima mwako,

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado