1 Monga ntchentche zakufa zimayika fungo loyipa mʼmafuta onunkhira,
2 Mtima wa munthu wanzeru umamutsogolera bwino,
3 Chitsiru ngakhale chikamayenda mu msewu,
4 Ngati wolamulira akukwiyira,
5 Pali choyipa chimene ndinachiona pansi pano,
6 Zitsiru amazipatsa ntchito zambiri zapamwamba,
7 Ndaona akapolo atakwera pa akavalo,
8 Amene amakumba dzenje adzagwamo yekha;
9 Amene amaphwanya miyala adzapwetekedwa ndi miyalayo;
10 Ngati nkhwangwa ili yobuntha
11 Nʼkopanda phindu kudziwa kuseweretsa njoka
12 Mawu a pakamwa pa munthu wanzeru ndi okondweretsa,
13 Chitsiru chimayamba ndi mawu opusa;
14 ndipo chitsiru chimachulukitsa mawu.
15 Chitsiru chimatopa msanga ndi ntchito yochepa;
16 Tsoka kwa iwe, iwe dziko ngati mfumu yako ikali mwana,
17 Wodala iwe, iwe dziko ngati mfumu yako ndi mwana wolemekezeka
18 Ngati munthu ndi waulesi, denga lake limaloshoka;
19 Phwando ndi lokondweretsa anthu,
20 Usanyoze mfumu ngakhale mu mtima mwako,