1 Uzikumbukira mlengi wako
2 Nthawi ya ukalamba wako, dzuwa ndi kuwala,
3 Nthawi imene manja ako adzanjenjemera,
4 Makutu ako adzatsekeka,
5 Imeneyi ndiyo nthawi imene anthu amaopa kupita kumalo okwera,
6 Kumbukira Iye chingwe cha siliva chisanaduke,
7 Iyi ndi nthawi imene thupi lidzabwerera ku dothi, kumene linachokera,
8 “Zopanda phindu! Zopandapake!” akutero Mlaliki.
9 Mlaliki sanali wozindikira zinthu kokha ayi, komanso ankaphunzitsa anthu. Iye ankasinkhasinkha ndi kufufuzafufuza ndi kulemba mwadongosolo miyambi yambiri.
10 Mlaliki anafufuzafufuza kuti apeze mawu oyenera, ndipo zimene analemba zinali zolondola ndiponso zoona.
11 Mawu a anthu anzeru ali ngati zisonga, zokamba zawo zimene anasonkhanitsa zili ngati misomali yokhomera, yoperekedwa ndi mʼbusa mmodzi.
12 Samalira mwana wanga, za kuwonjezera chilichonse pa zimenezi.
13 Basi zonse zamveka; mathero a nkhaniyi ndi awa:
14 Pakuti Mulungu adzaweruza zochita zonse,