Deuteronômio 33

NYA

1 Awa ndi madalitso amene Mose, munthu wa Mulungu, anawapereka kwa Aisraeli asanafe.

2 Iye anati:

3 Ndithu ndinu amene mumakonda anthu anu;

4 malamulo amene Mose anatipatsa,

5 Iye anali mfumu ya Yesuruni

6 “Lolani Rubeni akhale ndi moyo ndipo asafe,

7 Ndipo ponena za Yuda anati:

8 Za fuko la Alevi anati:

9 Iye ananena za abambo ake ndi amayi ake kuti,

10 Iye amaphunzitsa Yakobo malangizo anu

11 Inu Yehova, dalitsani luso lake lonse

12 Za fuko la Benjamini anati:

13 Za fuko la Yosefe anati:

14 ndi zinthu zambiri zimene zimacha ndi dzuwa

15 ndi zipatso zabwino kwambiri zochokera mʼmapiri amakedzanawa

16 ndi mphatso zabwino kwambiri zochokera pa dziko lapansi ndi zonse zimene zili mʼmenemo

17 Ulemerero wake uli ngati ngʼombe yayimuna yoyamba kubadwa;

18 Za fuko la Zebuloni anati:

19 Adzayitanira mitundu ya anthu kumapiri,

20 Za fuko la Gadi anati:

21 Iye anadzisankhira dziko labwino kwambiri;

22 Za fuko la Dani anati:

23 Za fuko la Nafutali anati:

24 Za fuko la Aseri anati:

25 Zotsekera za zipata zako zidzakhala za chitsulo ndi za mkuwa,

26 “Palibe wina wofanana ndi Mulungu wa Yesuruni,

27 Mulungu wamuyaya ndiye pothawirapo pathu,

28 Motero Israeli adzakhala yekha mwamtendere;

29 Iwe Israeli, ndiwe wodala!

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado