Cânticos 6

NYA

1 Iwe wokongola kuposa akazi onsewa,

2 Wachikondi wanga watsikira ku munda kwake,

3 Wokondedwa wangayo ndine wake ndipo iyeyo ndi wangawanga;

4 Ndiwe wokongola, bwenzi langa, ngati Tiriza,

5 Usandipenyetsetse;

6 Mano ako ali ngati gulu la nkhosa

7 Kukhalira kumbuyo kwa nsalu yako yophimba kumutu,

8 Ngakhale patakhala akazi a mfumu 60,

9 koma nkhunda yanga, wangwiro wanga ndi wosiyana ndi wina aliyense;

10 Ndani uyu akuoneka ngati mʼbandakucha,

11 Ndinatsikira ku munda wa mitengo ya alimondi

12 Ndisanazindikire kanthu,

13 Bwerera, bwerera iwe namwali wa ku Sulami;

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado