1 Iwe wokongola kuposa akazi onsewa,
2 Wachikondi wanga watsikira ku munda kwake,
3 Wokondedwa wangayo ndine wake ndipo iyeyo ndi wangawanga;
4 Ndiwe wokongola, bwenzi langa, ngati Tiriza,
5 Usandipenyetsetse;
6 Mano ako ali ngati gulu la nkhosa
7 Kukhalira kumbuyo kwa nsalu yako yophimba kumutu,
8 Ngakhale patakhala akazi a mfumu 60,
9 koma nkhunda yanga, wangwiro wanga ndi wosiyana ndi wina aliyense;
10 Ndani uyu akuoneka ngati mʼbandakucha,
11 Ndinatsikira ku munda wa mitengo ya alimondi
12 Ndisanazindikire kanthu,
13 Bwerera, bwerera iwe namwali wa ku Sulami;