Cânticos 7

NYA

1 Iwe namwali waufumu, mapazi ako ngokongola

2 Mchombo wako uli ngati chikho chowumbika bwino

3 Mawere ako akuoneka ngati ana awiri a mbawala,

4 Khosi lako lili see! ngati nsanja ya mnyanga wa njovu.

5 Mutu wako uli bwinobwino nengʼaa ngati phiri la Karimeli.

6 Ndiwe wokongola kwambiri ndiponso wosangalatsa,

7 Msinkhu wako uli ngati mtengo wa mgwalangwa,

8 Ndinati, “Ndikwera mtengo wa mgwalangwa;

9 ndipo pakamwa pako pali ngati vinyo wokoma kwambiri.

10 Wokondedwayo ine ndine wake,

11 Bwera wachikondi wanga, tiye tipite ku madera a ku midzi,

12 Tiye tilawirire mmamawa kupita ku minda ya mpesa,

13 Mitengo ya mankhwala a chisulo ikupereka fungo lake labwino,

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado