Cânticos 5

NYA

1 Ndalowa mʼmunda mwanga, iwe mlongo wanga, iwe mkwatibwi wanga;

2 Ndinagona tulo koma mtima wanga unali maso.

3 Ndavula kale zovala zanga,

4 Bwenzi langa anapisa dzanja lake pa chibowo cha pa chitseko;

5 Ndinanyamuka kukamutsekulira wachikondi wangayo,

6 Ndinamutsekulira wachikondi wanga,

7 Alonda anandipeza

8 Inu akazi a ku Yerusalemu ndithu ndikukupemphani,

9 Iwe wokongola kuposa akazi onsewa,

10 Wokondedwa wangayo ndi wowala kwambiri ndi wathanzi

11 Mutu wake ndi golide woyengeka bwino;

12 Maso ake ali ngati nkhunda

13 Masaya ake ali ngati timinda ta mbewu zokometsera zakudya

14 Manja ake ali ngati ndodo zagolide

15 Miyendo yake ili ngati mizati yamwala,

16 Milomo yake ndi yosangalatsa kwambiri;

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado