Cânticos 4

NYA

1 Ndiwe wokongoladi wokondedwa wanga!

2 Mano ako ali ngati gulu la nkhosa zomwe zangometedwa kumene,

3 Milomo yako ili ngati mbota yofiira;

4 Khosi lako lili ngati nsanja ya Davide,

5 Mawere ako ali ngati tiana tiwiri ta nswala,

6 Kamphepo kamadzulo kakayamba kuwuzira

7 Ndiwe wokongola kwambiri wokondedwa wanga;

8 Tiye tichoke ku Lebanoni iwe mkwatibwi wanga,

9 Iwe mlongo wanga, mkwatibwi wanga, wanditenga mtima,

10 Iwe mlongo wanga, mkwatibwi wanga, chikondi chako nʼchosangalatsa!

11 Iwe mkwatibwi wanga, milomo yako ikuchucha uchi ngati chisa cha njuchi;

12 Iwe mlongo wanga, mkwatibwi wanga, ndiwe munda wopiringidzidwa;

13 Zomera zako ndi munda wa zipatso za makangadza;

14 nadi ndi safiro,

15 Iwe ndiwe kasupe wa mʼmunda,

16 Dzuka, iwe mphepo yakumpoto,

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado