1 Ndiwe wokongoladi wokondedwa wanga!
2 Mano ako ali ngati gulu la nkhosa zomwe zangometedwa kumene,
3 Milomo yako ili ngati mbota yofiira;
4 Khosi lako lili ngati nsanja ya Davide,
5 Mawere ako ali ngati tiana tiwiri ta nswala,
6 Kamphepo kamadzulo kakayamba kuwuzira
7 Ndiwe wokongola kwambiri wokondedwa wanga;
8 Tiye tichoke ku Lebanoni iwe mkwatibwi wanga,
9 Iwe mlongo wanga, mkwatibwi wanga, wanditenga mtima,
10 Iwe mlongo wanga, mkwatibwi wanga, chikondi chako nʼchosangalatsa!
11 Iwe mkwatibwi wanga, milomo yako ikuchucha uchi ngati chisa cha njuchi;
12 Iwe mlongo wanga, mkwatibwi wanga, ndiwe munda wopiringidzidwa;
13 Zomera zako ndi munda wa zipatso za makangadza;
14 nadi ndi safiro,
15 Iwe ndiwe kasupe wa mʼmunda,
16 Dzuka, iwe mphepo yakumpoto,