1 Usiku wonse ndili pa bedi langa
2 Ndikudzuka tsopano ndipo ndidzayendayenda mu mzinda,
3 Alonda anandipeza
4 Nditawapitirira pangʼono
5 Inu akazi a ku Yerusalemu, ndithu ndikukupemphani
6 Kodi ndani amene akubwera kuchokera ku chipululu
7 Ona! Chimenecho ndi chonyamulira Solomoni,
8 onse atanyamula lupanga,
9 Mfumu Solomoni anadzipangira chonyamulirachi;
10 Milongoti yake anayipanga yasiliva,
11 Tukulani inu akazi a ku Ziyoni