1 Ine ndine duwa la ku Saroni,
2 Monga duwa lokongola pakati pa minga
3 Monga mtengo wa apulosi pakati pa mitengo ya mʼnkhalango
4 Iye wanditengera ku nyumba yaphwando,
5 Undidyetse keke ya mphesa zowuma,
6 Mutu wanga watsamira dzanja lake lamanzere,
7 Inu akazi a ku Yerusalemu, ndithu ndikukupemphani
8 Tamverani bwenzi langa!
9 Bwenzi langa ali ngati gwape kapena mwana wa mbawala.
10 Bwenzi langa anayankha ndipo anati kwa ine,
11 Ona, nyengo yozizira yatha;
12 Maluwa ayamba kuoneka pa dziko lapansi;
13 Mtengo wankhuyu ukubereka zipatso zake zoyambirira;
14 Nkhunda yanga yokhala mʼmingʼalu ya thanthwe,
15 Mutigwirire nkhandwe,
16 Bwenzi langa ndi wangadi ndipo ine ndine wake;
17 Kamphepo kamadzulo kakayamba kuwuzira