1 Ine ndinaona Ambuye atayima pambali pa guwa lansembe, ndipo anati:
2 Ngakhale atakumba pansi mpaka ku malo a anthu akufa,
3 Ngakhale atakabisala pamwamba pa phiri la Karimeli,
4 Ngakhale adani awo awakusire ku ukapolo,
5 Ambuye Yehova Wamphamvuzonse
6 Iye amene amamanga malo ake okhalamo kumwamba,
7 “Kodi kwa Ine, inu Aisraeli, simuli
8 “Taonani, maso a Ambuye Yehova
9 “Pakuti ndidzalamula,
10 Anthu onse ochimwa pakati pa anthu anga
11 “Tsiku limenelo ndidzabwezeretsa
12 kuti adzatengenso otsala a Edomu
13 Yehova akunena kuti
14 Ndidzawabwezeranso pabwino anthu anga Aisraeli;
15 Ndidzakhazika Aisraeli mʼdziko mwawo,