1 Masomphenya a Obadiya.
2 “Taona, ndidzakuchepetsani pakati pa anthu a mitundu ina;
3 Kudzikuza kwa mtima wako kwakusocheretsa,
4 Koma ngakhale umawuluka ngati chiwombankhanga
5 “Anthu akuba akanabwera kwa iwe,
6 Koma Esau adzalandidwa zinthu zonse,
7 Anthu onse ogwirizana nawo adzakupirikitsira kumalire;
8 Yehova akunena kuti, “Tsiku limenelo,
9 Ankhondo ako, iwe Temani, adzachita mantha,
10 Chifukwa cha nkhanza zimene unachitira mʼbale wako Yakobo,
11 Pamene adani
12 Iwe sunayenera kunyoza mʼbale wako
13 Iwe sunayenera kudutsa pa zipata za anthu anga
14 Sunayenera kudikirira pamphambano ya misewu
15 “Tsiku la Yehova layandikira
16 Iwe unamwa pa phiri langa loyera,
17 Koma pa Phiri la Ziyoni padzakhala chipulumutso;
18 Nyumba ya Yakobo idzasanduka moto
19 Anthu ochokera ku Negevi adzakhala
20 Aisraeli amene ali ku ukapolo
21 Opulumukawo adzapita ku Phiri la Ziyoni