Amós 8

NYA

1 Zimene Ambuye Yehova anandionetsa ndi izi: dengu la zipatso zakupsa.

2 Iye anandifunsa kuti, “Amosi nʼchiyani ukuona?”

3 “Tsiku limenelo,” Ambuye Yehova akulengeza kuti, “Nyimbo za mʼNyumba ya Mulungu zidzasanduka kulira kofuwula. Mitembo ya anthu idzachuluka, ndipo adzayiponya ponseponse! Kudzangoti zii!”

4 Imvani izi, inu amene mumapondereza anthu osowa

5 Mumanena kuti,

6 tigule osauka ndi ndalama zasiliva

7 Yehova amene Yakobo amamunyadira, walumbira kuti: Ine sindidzayiwala chilichonse chimene anachita.

8 “Kodi dziko silidzagwedezeka chifukwa cha zimenezi,

9 “Tsiku limenelo,” Ambuye Yehova akunena kuti,

10 Maphwando anu achipembedzo ndidzawasandutsa kulira kwa chisoni

11 “Nthawi ikubwera,” Ambuye Yehova akunena kuti,

12 Anthu azidzangoyendayenda kuchoka ku nyanja ina kupita ku nyanja ina.

13 “Tsiku limenelo

14 Onse amene amalumbira pa tchimo la Samariya,

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado