Amós 5

NYA

1 Israeli, imva mawu awa, nyimbo ya maliro imene ndikuyimba za iweyo:

2 “Namwali Israeli wagwa,

3 Ambuye Yehova akuti,

4 Zimene Yehova akunena kwa nyumba ya Israeli ndi izi:

5 musafunefune Beteli,

6 Funani Yehova kuti mukhale ndi moyo,

7 Inu amene mumasandutsa chiweruzo cholungama kukhala chowawa

8 (Iye amene analenga nyenyezi za Nsangwe ndi Akamwiniatsatana,

9 Iyeyo amabweretsa chiwonongeko modzidzimutsa pa anthu amphamvu

10 inu mumadana ndi amene amadzudzula mʼbwalo la milandu

11 Mumapondereza munthu wosauka

12 Pakuti Ine ndikudziwa kuchuluka kwa zolakwa zanu

13 Nʼchifukwa chake pa nthawi yotere munthu wanzeru sayankhulapo kanthu,

14 Muyike mtima wanu pa zabwino osati pa zoyipa,

15 Mudane ndi zoyipa, mukonde zabwino;

16 Choncho izi ndi zimene Ambuye, Yehova Mulungu Wamphamvuzonse, akunena:

17 Mʼminda yonse ya mpesa mudzakhala kulira kokhakokha,

18 Tsoka kwa inu amene mumalakalaka

19 Lidzakhala ngati tsiku limene munthu pothawa mkango

20 Kodi tsiku la Yehova silidzakhala mdima osati kuwala,

21 “Ndimadana nawo masiku anu achikondwerero ndipo ndimawanyoza;

22 Ngakhale mupereke nsembe zopsereza ndi nsembe zachakudya,

23 Musandisokose nazo nyimbo zanu!

24 Koma chiweruzo cholungama chiyende ngati madzi,

25 “Kodi pa zaka makumi anayi zimene munakhala mʼchipululu muja

26 Inu mwanyamula kachisi wa mfumu yanu,

27 Nʼchifukwa chake Ine ndidzakupititsani ku ukapolo, kutali kupitirira ku Damasiko,”

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado